Nyimbo 7:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ha, mapazi ako akongola m'zikwakwata,Mwana wamkaziwe wa mfumu!Pozinga m'cuuno mwako pakunga zonyezimira,Nchito ya manja a mmisiri waluso.

2. Pamcombo pako pakunga cikho coulungika,Cosasowamo vinyo wosanganika:Pamimba pako pakunga mulu wa tiriguWozingidwa ndi akakombo.

Nyimbo 7