Nyimbo 1:14-16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

14. Wokondedwa wanga ali kwa ine ngati cipukutu ca maluwa ofiiraM'minda yamipesa ya ku Engedi.

15. Taona, wakongolatu, bwenzi langa; namwaliwe taona, wakongola,Maso ako akunga a nkhunda.

16. Taona, wakongolatu, bwenzi langa, mnyamatawe, inde, wakongoletsa;Pogona pathu mpa msipu.

Nyimbo 1