Numeri 7:86 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Zipande zagolidi ndizo khumi ndi ziwiri, zodzala ndi cofukiza, cipande conse masekeli khumi, kuyesa sekeli wa malo opatulika; golidi wonse wa zipandezo ndiwo masekeli zana limodzi ndi makumi awiri;

Numeri 7

Numeri 7:76-89