Numeri 33:4-8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

4. pamene Aaigupto ailalikuika oyamba kubadwa ao onse, amene Yehova adawakantha; Yehova adaweruzanso milungu yao.

5. Ndipo ana a Israyeli macokera ku Ramese, nayenda namanga ku Sukoti.

6. Nacokera ku Sukoti, nayenda namanga m'Etamu, ndiko ku malekezero a cipululu.

7. Ndipo anacokera ku Etamu, nayenda nabwerera ku Pihahiroti, ndiko kutsogolo kwace kwa Baala Zefoni; namanga iwo patsogolo pa Migidoli.

8. Ndipo anacokera ku Pihahiroti, naoloka pakati pa nyanja nalowa m'cipululu; nayenda ulendo wa masiku atatu m'cipululu ca Etamu, namanga m'Mara.

Numeri 33