Numeri 32:34-38 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

34. Ndipo ana a Gadi anamanga Diboni, ndi Ataroti, ndi Aroeri;

35. Ataroti Sofani, Yazeri, ndi Yogebeha;

36. ndi Beti Nimira, ndi Beti Harani: midzi ya m'malinga, ndi makola a zoweta.

37. Ndipo ana a Rubeni anamanga Hesiboni, ndi Eleyali, ndi Kiriyataimu;

38. ndi Nebo, ndi Baala Meoni (nasintha maina ao), ndi Sibima; ndipo anaicha midzi adaimanga ndi maina ena.

Numeri 32