Numeri 23:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ananena fanizo lace, nati,Ku Aramu ananditenga Balaki,Mfumu ya Moabu ananditenga ku mapiri a kum'mawa;Idza, udzanditembererere Yakobo.Idza, nudzanyoze Israyeli.

Numeri 23

Numeri 23:5-17