Numeri 21:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Israyeli anamkantha ndi lupanga lakuthwa, nalanda dziko lace likhale lao lao, kuyambira Arinoni kufikira Yaboki, kufikira ana ai Amoni; popeza malire a ana a Amoni ndiwo olimba.

Numeri 21

Numeri 21:19-34