Numeri 21:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipitire pakati pa dziko lako; sitidzapatuka kulowa m'munda, kapena m'munda wampesa, sitidzamwako madzi a m'zitsime; tidzatsata mseu wacifumu, kufikira tapitirira malire ako.

Numeri 21

Numeri 21:21-23