Numeri 14:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

popeza anthu onse awa amene adaona ulemerero wanga, ndi zizindikilo zanga, ndidazicita m'Aigupto ndi m'cipululu, koma anandiyesa Ine kakhumi aka, osamvera mau anga;

Numeri 14

Numeri 14:20-31