Numeri 13:4-7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

4. Maina ao ndi awa: wa pfuko la Rubeni, Samuwa mwana wa Zakuri.

5. Wa pfuko la Simeoni, Safati mwana wa Hori.

6. Wa pfuko la Yuda, Kalebi mwana wa Yefune.

7. Wa pfuko la Isakara, Igali mwana wa Yosefe.

Numeri 13