12. Wa Dani, Ahiyezeri mwana wa Amisadai.
13. Wa Aseri, Pagiyeli mwana wa Okirani.
14. Wa Gadi, Eliyasafe mwana wa Deyueli.
15. Wa Nafitali, Ahira mwana wa Enani.
16. Iwo ndiwo oitanidwa a khamu, akalonga a mapfuko a makolo ao; ndiwo akuru a zikwizo za Israyeli.