Numeri 1:12-16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

12. Wa Dani, Ahiyezeri mwana wa Amisadai.

13. Wa Aseri, Pagiyeli mwana wa Okirani.

14. Wa Gadi, Eliyasafe mwana wa Deyueli.

15. Wa Nafitali, Ahira mwana wa Enani.

16. Iwo ndiwo oitanidwa a khamu, akalonga a mapfuko a makolo ao; ndiwo akuru a zikwizo za Israyeli.

Numeri 1