Nehemiya 8:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi msonkhano wonse wa iwo oturuka m'ndende anamanga misasa, nakhala m'misasamo; pakuti ciyambire masiku a Yesuwa mwana wa Nuni kufikira tsiku lija ana a Israyeli sanatero. Ndipo panali cimwemwe cacikuru.

Nehemiya 8

Nehemiya 8:7-18