Nehemiya 7:9-14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

9. Ana a Sefatiya, mazana atatu mphambu makumi asanu ndi awiri kudza awiri.

10. Ana a Ara, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.

11. Ana a Pakati Moabu, a ana a Yesuwa ndi Yoabu, zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi atatu kudza khumi limodzi ndi asanu ndi atatu.

12. Ana a Elamu, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri ndi makumi asanu kudza anai.

13. Ana a Zatu, mazana asanu ndi atatu mphambu makumi anai kudza asanu.

14. Ana a Zakai, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi asanu ndi limodzi.

Nehemiya 7