Nehemiya 7:64 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Awa anafunafuna maina ao m'buku la iwo owerengedwa mwa cibadwidwe, koma osawapeza; potero anawayesa odetsedwa, nawacotsa ku nchito ya nsembe.

Nehemiya 7

Nehemiya 7:54-73