Nehemiya 7:42-60 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

42. Ana a Harimu, cikwi cimodzi mphambu khumi limodzi kudza asanu ndi awiri.

43. A Levi: ana a Yesuwa, a Kadimiyeli, a ana a Hodeva, makumi asanu ndi awiri kudza anai.

44. Oyimbira: ana a Asafu, zana limodzi mphambu makumi anai kudza asanu ndi atatu.

45. Odikira: ana a Salumu, ana a Ateri, ana a Talimoni, ana a Akubu, ana a Hatita, ana a Sobai, zana limodzi mphambu makumi atatu kudza asanu ndi atatu.

46. Anetini: ana a Ziha, ana a Hasufa, ana a Tabaoti,

47. ana a Kerosi, ana a Siya, ana a Padoni,

48. ana a Lebana, ana a Hagaba, ana a Salimai,

49. ana a Hanani, ana a Gideri, ana a Gahara,

50. ana a Reaya, ana a Rezini, ana a Nekoda,

51. ana a Gazamu, ana a Uza, ana a Paseya,

52. ana a Besai, ana a Meunimu, ana a Nefusesimu,

53. ana a Bakibuki, ana a Hakufa, ana a Harihuri,

54. ana a Baziliti, ana a Mehida, ana a Harisa,

55. ana a Barikosi, ana a Sisera, ana a Tema,

56. ana a Neziya, ana a Hatifa.

57. Ana a akapolo a Solomo: ana a Sotai, ana a Sofereti, ana a Perida,

58. ana a Yaala, ana a Darikoni, ana a Gideli,

59. ana a Sefatiya, ana a Hatili, ana a Pokereti Hazebaimu, ana a Amoni.

60. Anetini onse, ndi ana a akapolo a Solomo, ndiwo mazana atatu mphambu makumi asanu ndi anai kudza awiri.

Nehemiya 7