Nehemiya 7:27-30 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

27. Amuna a ku Anatoti, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

28. Amuna a ku Bete-Azimaveti, makumi anai kudza awiri.

29. Amuna a ku Kiriyati Yearimu, Kefiira, ndi Beeroti, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi anai kudza atatu.

30. Amuna a ku Rama ndi Geba, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza mmodzi.

Nehemiya 7