Nehemiya 7:12-30 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

12. Ana a Elamu, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri ndi makumi asanu kudza anai.

13. Ana a Zatu, mazana asanu ndi atatu mphambu makumi anai kudza asanu.

14. Ana a Zakai, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi asanu ndi limodzi.

15. Ana a Binui, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi anai kudza asanu ndi atatu.

16. Ana a Betai, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

17. Ana a Azigadi, zikwi ziwiri mphambu mazana atatu kudza makumi awiri ndi awiri.

18. Ana a Adonikamu, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu ndi limodzi, kudza asanu ndi awiri.

19. Ana a Bigivai, zikwi ziwiri mphambu makumi asanu ndi limodzi kudza asanu ndi awiri.

20. Ana a Adini, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu kudza asanu.

21. Ana a Aberi, a Hezekiya, makumi asanu ndi anai kudza asanu ndi atatu.

22. Ana a Hasumu, mazana atatu mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

23. Ana a Bezai, mazana atatu mphambu makumi awiri kudza anai.

24. Ana a Harifi, zana limodzi mphambu khumi ndi awiri.

25. Ana a Gibeoni, makumi asanu ndi anai kudza asanu.

26. Amuna a ku Betelehemu ndi ku Netofa, zana limodzi mphambu makumi asanu ndi atatu kudza asanu ndi atatu.

27. Amuna a ku Anatoti, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

28. Amuna a ku Bete-Azimaveti, makumi anai kudza awiri.

29. Amuna a ku Kiriyati Yearimu, Kefiira, ndi Beeroti, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi anai kudza atatu.

30. Amuna a ku Rama ndi Geba, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza mmodzi.

Nehemiya 7