Nehemiya 7:12-17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

12. Ana a Elamu, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri ndi makumi asanu kudza anai.

13. Ana a Zatu, mazana asanu ndi atatu mphambu makumi anai kudza asanu.

14. Ana a Zakai, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi asanu ndi limodzi.

15. Ana a Binui, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi anai kudza asanu ndi atatu.

16. Ana a Betai, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

17. Ana a Azigadi, zikwi ziwiri mphambu mazana atatu kudza makumi awiri ndi awiri.

Nehemiya 7