Nehemiya 6:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti anafuna onse kutiopsa, ndi kuti, Manja ao adzaleka nchito, ndipo siidzacitika. Koma Inu, Mulungu, mulimbitse manja anga tsopano.

Nehemiya 6

Nehemiya 6:3-14