Nehemiya 3:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cipata ca kucigwa anacikonza Hanini; ndi okhala m'Zanowa anacimanga, naika zitseko zace, zokowera zace, ndi mipiringidzo yace; ndiponso mikono cikwi cimodzi ca lingalo mpaka ku cipata ca kudzala.

Nehemiya 3

Nehemiya 3:11-18