Nehemiya 13:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndinauza Alevi kuti adziyeretse, nabwere, nasunge pazipata kupatula dzuwa la Sabata. Mundikumbukire Icinso, Mulungu wanga, ndi kundileka monga mwa cifundo canu cacikuru.

Nehemiya 13

Nehemiya 13:14-30