Nehemiya 10:1-7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Okomera cizindikilo tsono ndiwo Nehemiya, Tirisata mwana wa Hakaliya, ndi Zedekiya,

2. Seraya, Agariya, Yeremiya,

3. Pasuri, Amariya, Malikiya,

4. Hatusi, Sebaniya, Maluki,

5. Harimu, Meremoti, Obadiya,

6. Danieli, Ginetoni, Baruki,

7. Mesulamu, Abiya, Miyamini,

Nehemiya 10