Nahumu 1:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yehova ndiye Mulungu wansanje, nabwezera cilango; Yehova ndiye wobwezera cilango, ndi waukali ndithu; Yehova ndiye wobwezera cilango oyambana naye, nasungira mkwiyo pa adani ace.

Nahumu 1

Nahumu 1:1-9