Nahumu 1:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova walamulira za iwe kuti asabzalidwenso ena a dzina lako; m'nyumba ya milungu yako ndidzacotsa fano losema ndi fano loyenga; ndidzakukonzerapo manda, pakuti iwe ndiwe wopepuka.

Nahumu 1

Nahumu 1:7-15