Mlaliki 7:4-7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

4. Mtima wa anzeru uli m'nyumba ya maliro; koma mtima wa zitsiru uli m'nyumba ya kuseka.

5. Kumva cidzudzulo ca anzeru kupambana kumva nyimbo ya zitsiru.

6. Pakuti kuseka kwa citsiru kunga minga irikutetheka pansi pa mphika; icinso ndi cabe.

7. Indetu nsautso iyarutsa wanzeru; ndi mtulo uipitsa mtima.

Mlaliki 7