Mlaliki 10:3-6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Inde, poyendanso citsiru panjira, nzeru yace imthera ndipo angoti kwa onse kuti, Ndine citsiru.

4. Ngati mkuru akukwiyira, usasiye malo ako; cifukwa cifatso cipembedza utacimwa kwambiri.

5. Pali coipa ndaciona pansi pano, ngati kulakwa koyambira ndi mkuru;

6. utsiru ukhazikika pamwamba penipeni, ndipo olemera angokhala mwamanyazi.

Mlaliki 10