Mlaliki 1:4-7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

4. Mbadwo wina opita, mbadwo wina nufika; koma dziko lingokhalabe masiku onse,

5. inde dzuwa lituruka, nililowa, nilifulumira komwe linaturukako.

6. Kulowa kumwela ndi kuzungulira: kumpoto zungulire zungulire imaomba mphepo; ibweranso monga mwa mazunguliridwe ace.

7. Mitsinje yonse ithira m'nyanja, koma nyanja yosadzala; komwe imukira mitsinjeyo, komweko ibweranso.

Mlaliki 1