Miyambi 8:2-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

2. Iima pamwamba pa mtunda,Pa mphambano za makwalala;

3. Pambali pa cipata polowera m'mudzi,Polowa anthu pa makomo ipfuula:

4. Ndinu ndikuitanani, amuna,Mau anga ndilankhula kwa ana a anthu.

5. Acibwana inu, cenjerani,Opusa inu, khalani ndi mtima wozindikira;

Miyambi 8