Miyambi 31:17-22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

17. Amanga m'cuuno mwace ndi mphamvu,Nalimbitsa mikono yace,

18. Azindikira kuti malonda ace ampindulira;Nyali yace sizima usiku.

19. Agwira njinga ya thonje ndi dzanja lace,Nafumbata mtengo wace.

20. Aolowera cikhato cace osauka;Natambasulira aumphawi manja ace.

21. Saopera banja lace cipale cofewa;Pakuti banja lace lonse libvala mlangali.

22. Adzipangira zimbwi zamaangamaanga;Nabvala bafuta ndi guta woti biriwiri.

Miyambi 31