Miyambi 31:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Mau a Lemueli mfumu, uthenga umene amace anamphunzitsa.

2. Ciani mwananga, Ciani mwana wa mimba yanga?Ciani mwana wa zowinda zanga?

3. Musapereke mphamvu yako kwa akazi,Ngakhale kuyenda m'njira yoononga mafumu.

Miyambi 31