Miyambi 30:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Mau a Aguri mwana wa Yake; uthenga. Munthuyo anati, Ndadzitopetsa, Mulungu;Ndadzitopetsa, Mulungu, ndathedwa;

2. Pakuti ndipambana anthu onse kupulukira,Ndiribe luntha la munthu.

3. Sindinaphunzira nzeruNgakhale kudziwa Woyerayo.

Miyambi 30