Miyambi 28:27-28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

27. Wogawira aumphawi sadzasowa;Koma wophimba maso ace adzatembereredwa kwambiri.

28. Pouka oipa anthu amabisala;Koma pakufa amenewo olungama acuruka.

Miyambi 28