18. Monga woyaruka woponya nsakali,Mibvi, ndi imfa,
19. Momwemo wonyenga mnzace ndi kuti, Ndi kusewera kumeneku.
20. Posowa nkhuni moto ungozima;Ndi popanda kazitape makangano angoleka.
21. Monga makala ozizira pa makala akunyeka, ndi nkhuni pamoto;Momwemo munthu wamakangano autsa ndeu.