27. Mzimu wa munthu ndiwo nyali ya Yehova;Usanthula m'kati monse mwa mimba.
28. Cifundo ndi ntheradi zisunga mfumu;Cifundo cicirikiza mpando wace.
29. Ulemerero wa anyamata ndiwo mphamvu yao;Kukongola kwa nkhalamba ndi
30. Mikwingwirima yopweteka icotsa zoipa;Ndi mikwapulo ilowa m'kati mwa mimba.