Miyambi 20:25-28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

25. Kunena mwansontho, ici ncopatulika, kuli msampha kwa munthu,Ndi kusinkhasinkha pambuyo pace atawinda.

26. Mfumu yanzeru ipeta amphulupulu,Niyendetsapo njinga ya gareta.

27. Mzimu wa munthu ndiwo nyali ya Yehova;Usanthula m'kati monse mwa mimba.

28. Cifundo ndi ntheradi zisunga mfumu;Cifundo cicirikiza mpando wace.

Miyambi 20