26. Wolanda za atate, ndi wopitikitsa amai,Ndiye mwana wocititsa manyazi ndi wogwetsa nkhope.
27. Ukangofuna, mwananga, kusocera kusiya mau akudziwitsa,Leka kumva mwambo.
28. Mboni yopanda pace inyoza ciweruzo;M'kamwa mwa amphulupulu mumeza zoipa,
29. Akonzera onyoza ciweruzo,Ndi mikwingwirima pamsana pa opusa.