18. Acibwana amalandira colowa ca utsiru;Koma ocenjera amabvala nzeru ngati korona.
19. Oipa amagwadira abwino,Ndi ocimwa pa makomo a olungama.
20. Waumphawi adedwa ndi anzace omwe;Koma akukonda wolemera acuruka.
21. Wonyoza anzace acimwa;Koma wocitira osauka cifundo adala.