Miyambi 13:9-12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

9. Kuunika kwa olungama kukondwa;Koma nyali ya oipa idzazima.

10. Kudzikuza kupikisanitsa;Koma omwe anauzidwa uphungu ali ndi nzeru.

11. Cuma colandiridwa mokangaza cidzacepa;Koma wokundika ndi dzanja adzaona zocuruka.

12. Ciyembekezo cozengereza cidwalitsa mtima;Koma pakufika cifuniroco ndico mtengo wa moyo.

Miyambi 13