Mika 3:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Momwemo Ziyoni adzalimidwa ngati: munda cifukwa ca inu, ndi m'Yerusalemu mudzasanduka miunda, ndi phiri la nyumba ngati misanje ya m'nkhalango.

Mika 3

Mika 3:5-12