Mateyu 9:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma kuti mudziwe kuti ali nazo mphamvu Mwana wa munthu pansi pano za kukhululukira macimo (pomwepo ananena kwa wodwalayo), Tanyamuka, nutenge chika lako, numuke kunyumba kwako.

Mateyu 9

Mateyu 9:3-15