Mateyu 6:9-13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

9. Cifukwa cace pempherani inu comweci:Atate wathu wa Kumwamba, Dzina lanu liyeretsedwe.

10. Ufumu wanu udze. Kufuna kwanu kucitidwe, monga Kumwamba comweco pansi pano.

11. Mutipatse ife lero cakudya cathu calero.

12. Ndipo mutikhululukire mangawa athu, monga ifenso takhululukira amangawa anthu.

13. Ndipo musatitengere kokatiyesa, koma mutipulumutse kwa woipayo.

Mateyu 6