Mateyu 5:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Fulumira kuyanjana ndi mnzako wamlandu, pamene uli naye panjira; kapena mnzako wamlandu angakupereke iwe kwa woweruza mlandu, ndi woweruzayo angapereke iwe kwa msilikari, nuponyedwe iwe m'nyumba yandende.

Mateyu 5

Mateyu 5:19-29