Mateyu 3:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo masiku aja anadza Yohane Mbatizi, nalalikira m'cipululu ca Yudeya,

2. nanena, Tembenukani mitima; cifukwa Ufumu wa Kumwamba wayandikira.

Mateyu 3