3. Pakuti opusawo, m'mene anatenga nyali zao, sanadzitengeranso mafuta;
4. koma anzeruwo anatenga mafuta m'nsupa zao, pamodzi ndi nyali zao.
5. Ndipo pamene mkwati anacedwa, onsewo anaodzera, nagona tulo.
6. Koma pakati pa usiku panali kupfuula, Onani, mkwati! turukani kukakomana naye.