Mateyu 23:35 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

kotero kuti udzafika pa inu mwazi wonse wotayidwa pa dziko lapansi, kuyambira ku mwazi wa Abele wolungamayo, kufikira ku mwazi wa Zakariya mwana wa Barakiya, amene munamupha pakati pa Kacisi ndi guwa la nsembe.

Mateyu 23

Mateyu 23:32-39