Mateyu 21:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mipingo yakumtsogolera ndi yakumtsatira, inapfuula, kuti, Hosana kwa Mwana wa Davide! Wolemekezeka ndiye wakudza m'dzina la Ambuye! Hosana m'Kumwambamwamba!

Mateyu 21

Mateyu 21:1-16