Mateyu 21:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ubatizo wa Yohane, ucokera kuti? Kumwamba kodi kapena kwa anthu? Koma iwo anafunsana wina ndi mnzace, kuti, Tikati, Kumwamba, Iye adzati kwa ife, Munalekeranji kumvera iye?

Mateyu 21

Mateyu 21:24-26