Mateyu 20:30 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo onani, anthu akhungu awiri anakhala m'rnphepete mwa njira; m'mene iwo anamva kuti Yesu analikupitirirapo, anapfuula nati, Muticitire ife cifundo, Inu Mwana wa Davide.

Mateyu 20

Mateyu 20:27-32