Mateyu 19:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo panali pamene Yesu anatha mau amenewa, anacokera ku Galileya, nadza ku malire a Yudeya, a ku tsidya lija la Yordano.

2. Ndipo makamu akuru a anthu anamtsata; ndipo Iye anawaciritsa kumeneko.

Mateyu 19