Mateyu 13:33 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Fanizo lina ananena kwa iwo; Ufumu wa Kumwamba uli wofanafana ndi cotupitsa mikate, cimene mkazi anacitenga, nacibisa m'miyeso itatu ya ufa, kufikira wonse unatupa.

Mateyu 13

Mateyu 13:31-40